Danieli 11:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndipo chaka choyamba cha Dariyo Mmedi ine Mikayeli ndinabwera kumuthandiza ndi kumuteteza Gabrieli. Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa. Onani mutuwo |