Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 11:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndipo chaka choyamba cha Dariyo Mmedi ine Mikayeli ndinabwera kumuthandiza ndi kumuteteza Gabrieli.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 11:1
6 Mawu Ofanana  

Tamandani Yehova, inu angelo ake, amphamvu inu amene mumachita zimene amalamula, amene mumamvera mawu ake.


Kenaka wooneka ngati munthu uja anandikhudzanso ndipo anandipatsa mphamvu.


ndipo Dariyo Mmedi analanda ufumuwo ali ndi zaka 62.


Kunamukomera Dariyo kusankha akalonga 120 kuti alamulire mu ufumu wonse,


Mʼchaka choyamba cha Dariyo mwana wa Ahasiwero (wochokera kwa Amedi), amene anakhala mfumu ya ku Babuloni,


Kumeneko analimbikitsa mitima ya ophunzira ndi kuwapatsa mphamvu kuti akhalebe woona mʼchikhulupiriro. Iwo anati, “Ife tiyenera kudutsa mʼmasautso ambiri kuti tikalowe mu ufumu wa Mulungu.”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa