2 Samueli 2:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Davide anatenganso anthu amene anali nawo aliyense ndi banja lake, ndipo anakakhala ku midzi ya ku Hebroni. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo Davide anakwera nao anyamata ake okhala naye, munthu yense ndi banja lake; iwowa nakhala m'midzi ya Hebroni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Davide anakwera nao anyamata ake okhala naye, munthu yense ndi banja lake; iwowa nakhala m'midzi ya Hebroni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndipo Davide adabwera ndi anthu ake aja amene anali nawo, aliyense ndi banja lake. Adakhala m'midzi ya ku Hebroni. Onani mutuwo |