Zekariya 8:8 - Buku Lopatulika8 ndipo ndidzabwera nao, nadzakhala m'kati mwa Yerusalemu; ndipo iwo adzakhala anthu anga, nanenanso ndidzakhala Mulungu wao, m'choonadi ndi m'chilungamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndipo ndidzabwera nao, nadzakhala m'kati mwa Yerusalemu; ndipo iwo adzakhala anthu anga, nanenanso ndidzakhala Mulungu wao, m'choonadi ndi m'chilungamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndidzaŵabweza kuti akhalenso ku Yerusalemu. Pamenepo adzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wao, wokhulupirika ndi wolungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndidzawabweretsa kuti adzakhale mu Yerusalemu; adzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo, wokhulupirika ndi wolungama pakati pawo.” Onani mutuwo |