Zekariya 8:12 - Buku Lopatulika12 Pakuti padzakhala mbeu ya mtendere; mpesa udzapatsa zipatso zake, ndi nthaka idzapatsa zobala zake, ndi miyamba idzapatsa mame ao; ndipo ndidzalandiritsa otsala a anthu awa izi zonse, chikhale cholowa chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pakuti padzakhala mbeu ya mtendere; mpesa udzapatsa zipatso zake, ndi nthaka idzapatsa zobala zake, ndi miyamba idzapata mame ao; ndipo ndidzalandiritsa otsala a anthu awa izi zonse, chikhale cholowa chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Adzabzala mwamtendere, mpesa udzabala zipatso zake, ndipo nthaka idzabereka kwambiri. Mvula idzagwa kuchokera kumwamba. Madalitso onseŵa ndidzaŵapatsa otsala mwa anthuŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Pakuti mbewu zidzamera bwino, mpesa udzabala zipatso zake, nthaka idzatulutsa zomera zake, ndi thambo lidzagwetsa mame. Ndidzapereka zonse kukhala cholowa cha otsala mwa anthu awa. Onani mutuwo |