Zekariya 8:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti asanafike masiku aja, panalibe kulipidwira munthu, kapena kulipidwira nyama, ndipo analibe mtendere iye wakutuluka, kapena wakulowa, chifukwa cha wosautsa; pakuti ndinatumiza munthu yense atsutsane naye mnzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti asanafike masiku aja, panalibe kulipidwira munthu, kapena kulipidwira nyama, ndipo analibe mtendere iye wakutuluka, kapena wakulowa, chifukwa cha wosautsa; pakuti ndinatumiza munthu yense atsutsane naye mnzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mpaka nthaŵi imeneyo panalibe wina wolandirapo malipiro pa ntchito kapena wopindulapo pa zoŵeta. Panalibe munthu amene ankadziyendera mwamtendere, chifukwa cha adani, popeza kuti anthu onse ndidaaŵayambanitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mpaka nthawi imeneyi panalibe munthu wolandira malipiro pa ntchito kapena ndalama zolipirira nyama zogwira ntchito. Panalibe munthu amene ankadzigwirira ntchito mwamtendere chifukwa choopa adani ake, pakuti Ine ndinkawayambanitsa. Onani mutuwo |