Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 8:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta Wamphamvuzonse adandipatsanso uthenga uwu wakuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Awa ndi mawu amene Yehova Wamphamvuzonse ananena.

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 8:1
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,


koma ndidzawabalalitsa ndi kamvulumvulu mwa amitundu onse amene sanawadziwe. Motero dziko linakhala bwinja, m'mbuyo mwao; palibe munthu wopitapo ndi kubwererako; pakuti adaika dziko lofunikalo labwinja.


Atero Yehova wa makamu: Ndimchitira nsanje Ziyoni ndi nsanje yaikulu, ndipo ndimchitira nsanje ndi ukali waukulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa