Zekariya 7:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo a ku Betele anatuma Sarezere ndi Regemumeleke ndi anthu ao, apepeze Yehova, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo a ku Betele anatuma Sarezere ndi Regemumeleke ndi anthu ao, apepeze Yehova, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anthu a ku Betele anali atatuma Sarezere ndi Regemumeleki ndi anthu ao, kuti akapemphe chifundo kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anthu a ku Beteli anali atatuma Sarezeri ndi Regemu-Meleki pamodzi ndi anthu awo, kuti akapemphe chifundo kwa Yehova Onani mutuwo |