Zekariya 7:11 - Buku Lopatulika11 Koma anakana kumvera, nakaniza phewa lao, natseka makutu ao, kuti asamve. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma anakana kumvera, nakaniza phewa lao, natseka makutu ao, kuti asamve. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Koma iwowo adakana kumvera, adandifulatira ndi mtima wokanika. Adatseka makutu ao kuti asamve. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Koma makolo anu anakana kumvera uthenga umenewu; anawumitsa mtima nandifulatira, natseka makutu awo kuti asamve. Onani mutuwo |