Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 4:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Chauta adandipatsanso uthenga uwu wakuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndipo Yehova anayankhulanso nane kuti,

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 4:8
3 Mawu Ofanana  

Ndiwe yani, phiri lalikulu iwe? Pamaso pa Zerubabele udzasanduka chidikha; ndipo adzatulutsa mwala woikidwa pamwamba, ndi kufuula, Chisomo, chisomo nao.


Manja a Zerubabele anaika maziko a nyumba iyi, manja ake omwe adzaitsiriza; ndipo udzadziwa kuti Yehova wa makamu anandituma kwa inu.


Ndipo iwo akukhala kutali adzafika, nadzamanga ku Kachisi wa Yehova, ndipo inu mudzadziwa kuti Yehova wa makamu ananditumiza kwa inu. Ndipo ichi chidzachitika ngati mudzamvera mwachangu mau a Yehova Mulungu wanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa