Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 3:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo mthenga wa Yehova anamchitira Yoswa umboni, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo mthenga wa Yehova anamchitira Yoswa umboni, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Mngelo wa Chauta uja adauza Yoswa kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Mngelo wa Yehova analimbikitsa Yoswa kuti,

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 3:6
11 Mawu Ofanana  

M'mazunzo ao onse Iye anazunzidwa, ndipo mthenga wakuimirira pamaso pake anawapulumutsa; m'kukonda kwake ndi m'chisoni chake Iye anawaombola, nawabereka nawanyamula masiku onse akale.


Pakuti ndinatsimikizitsa kwa atate anu tsiku lomwe ndinawatulutsa iwo kudziko la Ejipito, mpaka lero lomwe, kuuka mamawa ndi kutsimikiza, kuti, Mverani mau anga.


inde, analimbana ndi wamthenga nampambana; analira, nampembedza Iye; anampeza Iye ku Betele, ndi kumeneko Iye analankhula ndi ife;


Pamenepo anandionetsa Yoswa mkulu wa ansembe alikuima pamaso pa mthenga wa Yehova, ndi Satana alikuima padzanja lake lamanja, atsutsana naye.


Ndipo ndinati, Amuike nduwira yoyera pamutu pake. Naika nduwira yoyera pamutu pake, namveka ndi zovala; ndi mthenga wa Yehova anaimirirapo.


Atero Yehova wa makamu: Ukadzayenda m'njira zanga, ndi kusunga udikiro wanga, pamenepo udzaweruza nyumba yanga, ndi kusunga mabwalo anga, ndipo ndidzakupatsa malo oyendamo mwa awa oimirirapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa