Zekariya 14:3 - Buku Lopatulika3 Pamenepo Yehova adzatuluka, nadzachita nkhondo ndi amitundu aja, monga anachitira nkhondo tsiku lakudumana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamenepo Yehova adzatuluka, nadzachita nkhondo ndi amitundu aja, monga anachitira nkhondo tsiku lakudumana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pambuyo pake Chauta adzabwera kudzamenyana ndi adani amenewo, monga m'mene amachitira pa tsiku la nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamenepo Yehova adzabwera kudzamenyana ndi mitundu ya anthu imeneyi, ngati mmene amachitira pa nthawi ya nkhondo. Onani mutuwo |