Zekariya 12:1 - Buku Lopatulika1 Katundu wa mau a Yehova wakunena Israele. Atero Yehova, wakuyala miyamba, ndi kuika maziko a dziko lapansi, ndi kulenga mzimu wa munthu m'kati mwake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Katundu wa mau a Yehova wakunena Israele. Atero Yehova, wakuyala miyamba, ndi kuika maziko a dziko lapansi, ndi kulenga mzimu wa munthu m'kati mwake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mau a Chauta onena za Israele. Chauta ndiye adayala mlengalenga ndi kukhazikitsa dziko lapansi, ndiyenso amene adalenga mpweya wokhala mwa munthu. Iye akunena kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Uthenga wa Yehova kwa Israeli. Yehova, amene amayala mlengalenga, amene amayika maziko a dziko lapansi, ndiponso amene amalenga mzimu wokhala mwa munthu, akunena kuti, Onani mutuwo |