Zekariya 11:17 - Buku Lopatulika17 Tsoka mbusa wopanda pake, wakusiya zoweta! Lupanga padzanja lake, ndi pa diso lake la kumanja; dzanja lake lidzauma konse, ndi diso lake lamanja lidzada bii. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Tsoka mbusa wopanda pake, wakusiya zoweta! Lupanga pa dzanja lake, ndi pa diso lake la kumanja; dzanja lake lidzauma konse, ndi diso lake lamanja lidzada bii. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Tsoka kwa mbusa wanga wopandapakeyo, amene amasiya nkhosa! Amkanthe ndi lupanga pa mkono, ndi pa diso lake lakumanja. Mkono wakewo ufwape, ndipo diso lakelo lichite khungu kotheratu!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “Tsoka kwa mʼbusa wopandapake, amene amasiya nkhosa! Lupanga limukanthe pa mkono wake ndi pa diso lake lakumanja! Mkono wake ufote kotheratu, diso lake lamanja lisaonenso.” Onani mutuwo |