Zefaniya 3:18 - Buku Lopatulika18 Ndidzasonkhanitsa iwo akulirira msonkhano woikika, ndiwo a mwa iwe, amene katundu wake anawakhalira mtonzo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndidzasonkhanitsa iwo akulirira msonkhano woikika, ndiwo a mwa iwe, amene katundu wake anawakhalira mtonzo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Monga pa masiku achikondwerero, ndidzakuchotsera tsoka, limene lingokuvutitsa ndi kukunyozetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Ndidzakuchotserani zowawa za pa zikondwerero zoyikika; nʼzolemetsa ndi zochititsa manyazi. Onani mutuwo |