Zefaniya 3:19 - Buku Lopatulika19 Taonani, nthawi yomweyo ndidzachita nao onse akuzunza iwe; ndipo ndidzapulumutsa wotsimphinayo, ndi kusonkhanitsa wopirikitsidwayo; ndipo ndidzawaika akhale chilemekezo ndi dzina, iwo amene manyazi ao anali m'dziko lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Taonani, nthawi yomweyo ndidzachita nao onse akuzunza iwe; ndipo ndidzapulumutsa wotsimphinayo, ndi kusonkhanitsa wopirikitsidwayo; ndipo ndidzawaika akhale chilemekezo ndi dzina, iwo amene manyazi ao anali m'dziko lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Nthaŵi imeneyo ndidzaŵakhaulitsa onse amene amakuzunzani. Ndidzapulumutsa otayika ndi kusonkhanitsa onse obalalika. Ndidzaŵatamanda ndi kuŵapatsa ulemu, kulikonse kumene adani ao ankaŵachititsa manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Taonani, nthawi imeneyo ndidzathana ndi onse amene anakuponderezani; ndidzapulumutsa olumala ndi kusonkhanitsa amene anamwazika. Ndidzawayamikira ndi kuwachitira ulemu mʼdziko lililonse mmene anachititsidwa manyazi. Onani mutuwo |