Zefaniya 3:1 - Buku Lopatulika1 Tsoka uyo wopanduka, ndi wodetsedwa, ndiye mzinda wozunza! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tsoka uyo wopanduka, ndi wodetsedwa, ndiye mudzi wozunza! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsoka kwa Yerusalemu, mzinda wopanduka, wonyansa ndi wankhanza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsoka kwa mzinda wa anthu opondereza, owukira ndi odetsedwa! Onani mutuwo |