Zefaniya 2:8 - Buku Lopatulika8 Ndinamva kutonza kwa Mowabu ndi matukwano a ana a Amoni, zimene anatonza nazo anthu anga, ndi kudzikuza pa malire ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndinamva kutonza kwa Mowabu ndi matukwano a ana a Amoni, zimene anatonza nazo anthu anga, ndi kudzikuza pa malire ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta akuti, “Ndamva kunyoza kwa Amowabu, ndiponso kutukwana kwa Aamoni, m'mene anyozera anthu anga ndi m'mene adzikuzira m'dziko mwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Ndamva kunyoza kwa Mowabu ndi chipongwe cha Amoni, amene ananyoza anthu anga ndi kuopseza kuti alanda dziko lawo. Onani mutuwo |