Zefaniya 2:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo dziko la kunyanja lidzakhala busa, ndi mapanga a abusa, ndi makola a zoweta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo dziko la kunyanja lidzakhala busa, ndi mapanga a abusa, ndi makola a zoweta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Dziko limene lili m'mphepete mwa nyanja, lidzasanduka madambo a abusa, ndi makola a nkhosa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Dziko la mʼmbali mwa nyanja, kumene kumakhala Akereti, lidzakhala malo a abusa ndi la makola a nkhosa. Onani mutuwo |