Zefaniya 1:3 - Buku Lopatulika3 Ndidzatha munthu ndi nyama; ndidzatha mbalame za m'mlengalenga, ndi nsomba za m'nyanja, ndi zokhumudwitsa pamodzi ndi oipa; ndipo ndidzaononga anthu kuwachotsa panthaka, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndidzatha munthu ndi nyama; ndidzatha mbalame za m'mlengalenga, ndi nsomba za m'nyanja, ndi zokhumudwitsa pamodzi ndi oipa; ndipo ndidzaononga anthu kuwachotsa panthaka, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Ndidzafafaniziratu anthu ndi nyama zomwe. Ndidzaononga mbalame zamumlengalenga ndi nsomba zam'nyanja. Ndidzagwetsa anthu ochimwa. Ndidzafafaniziratu mtundu wa anthu kuti usaonekenso pa dziko lapansi,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Ndidzawononga anthu pamodzi ndi nyama zomwe; ndidzawononga mbalame zamlengalenga ndi nsomba za mʼnyanja. Ndidzawononga anthu oyipa, ndipo ndidzafafaniza mtundu wa anthu pa dziko lonse lapansi,” akutero Yehova. Onani mutuwo |