Yoweli 3:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo anachitira anthu anga maere, napereka mwana wamwamuna kusinthana ndi mkazi wadama, nagula vinyo ndi mwana wamkazi kuti amwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anachitira anthu anga maere, napereka mwana wamwamuna kusinthana ndi mkazi wadama, nagula vinyo ndi mwana wamkazi kuti amwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adagaŵana anthu anga pochita maere, mnyamata adamsinthitsa ndi mkazi wadama, mtsikana nkumsinthitsa ndi vinyo, kenaka adamumwa vinyoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anagawana anthu anga pochita maere ndipo anyamata anawasinthanitsa ndi akazi achiwerewere; anagulitsa atsikana chifukwa cha vinyo kuti iwo amwe. Onani mutuwo |