Yoweli 3:17 - Buku Lopatulika17 Momwemo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu wakukhala mu Ziyoni, phiri langa lopatulika; pamenepo Yerusalemu adzakhala wopatulika, osapitanso alendo pakati pake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Momwemo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu wakukhala m'Ziyoni, phiri langa lopatulika; pamenepo Yerusalemu adzakhala wopatulika, osapitanso alendo pakati pake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Motero mudzadziŵa kuti ndine Chauta, Mulungu wanu, amene ndimakhala ku Ziyoni, ku phiri langa loyera. Yerusalemu adzakhala woyera ndipo alendo sadzamthiranso nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine Yehova Mulungu wanu, ndimakhala mu Ziyoni, phiri langa lopatulika. Yerusalemu adzakhala wopatulika; alendo sadzamuthiranso nkhondo. Onani mutuwo |