Yoweli 3:14 - Buku Lopatulika14 Aunyinji, aunyinji m'chigwa chotsirizira mlandu! Pakuti layandikira tsiku la Yehova m'chigwa chotsirizira mlandu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Aunyinji, aunyinji m'chigwa chotsirizira mlandu! Pakuti layandikira tsiku la Yehova m'chigwa chotsirizira mlandu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Makamu ndi makamu a anthu ali m'Chigwa cha Chiweruzo. Ndithu tsiku la Chauta layandikira m'Chigwa cha Chiweruzo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Chigulu cha anthu, chigulu cha anthu, mʼchigwa cha chiweruzo! Pakuti tsiku la Yehova layandikira mʼchigwa cha chiweruzo. Onani mutuwo |