Yoweli 3:10 - Buku Lopatulika10 Sulani makasu anu akhale malupanga, ndi zikwakwa zanu zikhale nthungo; wofooka anene, Ndine wamphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Sulani makasu anu akhale malupanga, ndi zikwakwa zanu zikhale nthungo; wofooka anene, Ndine wamphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Sulani makasu anu kuti akhale malupanga. Sulani migwandali yanu kuti ikhale mikondo. Ngakhale wofooka anene kuti, Ndalimba mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Sulani makasu anu kuti akhale malupanga ndipo zikwanje zanu zikhale mikondo. Munthu wofowoka anene kuti, “Ndine wamphamvu!” Onani mutuwo |