Yoweli 3:1 - Buku Lopatulika1 Pakuti taonani, masiku awo, ndi nthawi iyo, pamene ndibwera nao andende a Yuda ndi a Yerusalemu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pakuti taonani, masiku awo, ndi nthawi iyo, pamene ndibwera nao andende a Yuda ndi a Yerusalemu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Nthaŵi imeneyo itafika, masiku amene ndidzakwezanso anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Masiku amenewo ndiponso nthawi imeneyo, nditadzabwezeretsanso Yerusalemu ndi Yuda mʼchimake, Onani mutuwo |