Yoweli 2:29 - Buku Lopatulika29 ndi pa akapolo ndi adzakazi omwe ndidzatsanulira mzimu wanga masiku awo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 ndi pa akapolo ndi adzakazi omwe ndidzatsanulira mzimu wanga masiku awo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Masiku amenewo, ndidzatsitsa mzimu wanga ngakhale pa akapolo ndi pa adzakazi omwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ngakhalenso pa antchito anga aamuna ndi aakazi ndidzakhuthulira Mzimu wanga masiku amenewo. Onani mutuwo |