Yoweli 2:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo mudzadziwa kuti Ine ndili pakati pa Israele, ndi kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu, palibe wina; ndi anthu anga sadzachita manyazi nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo mudzadziwa kuti Ine ndili pakati pa Israele, ndi kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu, palibe wina; ndi anthu anga sadzachita manyazi nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Mudzadziŵa kuti Ine ndili naye Israele, ndipo kuti Ine ndekha, osati wina, ndine Chauta, Mulungu wanu. Anthu anga sadzaŵanyozanso ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndili mu Israeli, kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu, ndi kuti palibenso wina; ndipo anthu anga sadzachitanso manyazi. Onani mutuwo |