Yoweli 2:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo mudzadyaidya ndi kukhuta, nimudzalemekeza dzina la Yehova Mulungu wanu, amene anachita nanu modabwitsa; ndi anthu anga sadzachita manyazi nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo mudzadyaidya ndi kukhuta, nimudzalemekeza dzina la Yehova Mulungu wanu, amene anachita nanu modabwitsa; ndi anthu anga sadzachita manyazi nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 “Mudzadya zambiri ndi kukhuta, ndipo mudzatamanda dzina la Chauta, Mulungu wanu, amene wakuchitirani zodabwitsa. Choncho anthu anga sadzaŵanyozanso ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Mudzakhala ndi chakudya chambiri, mpaka mudzakhuta, ndipo mudzatamanda dzina la Yehova Mulungu wanu, amene wakuchitirani zodabwitsa; ndipo anthu anga sadzachitanso manyazi. Onani mutuwo |