Yoweli 2:22 - Buku Lopatulika22 Musamaopa, nyama zakuthengo inu; pakuti m'chipululu muphukanso msipu; pakuti mitengo ibala zipatso zao; mikuyu ndi mipesa ipatsa mphamvu zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Musamaopa, nyama zakuthengo inu; pakuti m'chipululu muphukanso msipu; pakuti mitengo ibala zipatso zao; mikuyu ndi mipesa ipatsa mphamvu zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Inu nyama zakuthengo, musaope, pakuti msipu wakuchipululu akuphukira. Mitengo ikubala zipatso. Mkuyu ndi mpesa zikubereka kwamphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Inu nyama zakuthengo, musachite mantha, pakuti msipu wa ku chipululu ukuphukira. Mitengo ikubala zipatso zake; mitengo ya mkuyu ndi mpesa ikubereka kwambiri. Onani mutuwo |