Yoweli 2:18 - Buku Lopatulika18 Pamenepo Yehova anachitira dziko lake nsanje, nachitira anthu ake chifundo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pamenepo Yehova anachitira dziko lake nsanje, nachitira anthu ake chifundo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Apo chikondi cha Chauta chidayaka ngati moto chifukwa cha dziko lake, ndipo adaŵachitira chifundo anthu ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pamenepo Yehova adzachitira nsanje dziko lake ndi kuchitira chisoni anthu ake. Onani mutuwo |