Yoweli 2:15 - Buku Lopatulika15 Ombani lipenga mu Ziyoni, patulani tsiku losala, lalikirani msonkhano woletsa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ombani lipenga m'Ziyoni, patulani tsiku losala, lalikirani msonkhano woletsa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Lizani lipenga ku Ziyoni. Lengezani mwambo wa kusala zakudya. Muitanitse msonkhano waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Lizani lipenga mu Ziyoni, lengezani tsiku losala zakudya, itanitsani msonkhano wopatulika. Onani mutuwo |