Yoswa 1:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo atafa Mose mtumiki wa Yehova, Yehova anati kwa Yoswa mwana wa Nuni mnyamata wa Mose, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo atafa Mose mtumiki wa Yehova, Yehova anati kwa Yoswa mwana wa Nuni mnyamata wa Mose, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mose, mtumiki wa Chauta, atamwalira, Chauta adalankhula ndi mthandizi wake wa Moseyo, dzina lake Yoswa, mwana wa Nuni, kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Atamwalira Mose mtumiki wa Mulungu, Yehova anati kwa Yoswa mwana wa Nuni mthandizi wa Mose: Onani mutuwo |