Yona 1:4 - Buku Lopatulika4 Koma Yehova anautsa chimphepo chachikulu panyanja, ndipo panali namondwe wamkulu panyanja, ndi chombo chikadasweka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma Yehova anautsa chimphepo chachikulu panyanja, ndipo panali namondwe wamkulu panyanja, ndi chombo chikadasweka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma Chauta adautsa namondwe, ndipo nyanja idayamba kuŵinduka kwambiri ndi namondweyo, kotero kuti chombo chinali pafupi kuwonongeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma Yehova anatumiza chimphepo champhamvu pa nyanja, ndipo panauka namondwe wamphamvu amene anafuna kuphwanya sitimayo. Onani mutuwo |