Yona 1:2 - Buku Lopatulika2 Nyamuka, pita ku Ninive, mzinda waukuluwo, nulalikire motsutsana nao; pakuti choipa chao chandikwerera pamaso panga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nyamuka, pita ku Ninive, mudzi waukuluwo, nulalikire motsutsana nao; pakuti choipa chao chandikwerera pamaso panga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Nyamuka, upite ku Ninive, mzinda waukulu uja. Ukaŵadzudzule momveka ndithu anthu chifukwa ndaona kuipa kwao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Nyamuka, pita ku mzinda waukulu wa Ninive ndipo ukalalikire motsutsana nawo, chifukwa zoyipa zawo zafika pamaso panga.” Onani mutuwo |