Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yona 1:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona mwana wa Amitai, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona mwana wa Amitai, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tsiku lina Chauta adapatsa Yona, mwana wa Amitai, uthenga uwu wakuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anayankhula ndi Yona mwana wa Amitai kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yona 1:1
7 Mawu Ofanana  

Anabweza malire a Israele kuyambira polowera ku Hamati mpaka ku Nyanja ya Araba, monga mwa mau a Yehova Mulungu wa Israele, amene ananena ndi dzanja la mtumiki wake Yona mwana wa Amitai mneneriyo, ndiye wa Gatihefere.


Mkango ukabangula, ndani amene saopa? Ambuye Yehova wanena, ndani amene sanenera?


Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona nthawi yachiwiri, ndi kuti,


Obadwa oipa ndi achigololo afunafuna chizindikiro; ndipo sadzalandira chizindikiro china, koma chizindikiro cha Yona. Ndipo Iye anawasiya, nachokapo.


Amuna a ku Ninive adzaimirira pa mlandu wotsiriza pamodzi ndi anthu a mbadwo uno, nadzawatsutsa; pakuti iwo analapa pa kulalikira kwa Yona; ndipo onani, wakuposa Yona ali pano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa