Yona 1:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona mwana wa Amitai, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona mwana wa Amitai, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsiku lina Chauta adapatsa Yona, mwana wa Amitai, uthenga uwu wakuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anayankhula ndi Yona mwana wa Amitai kuti, Onani mutuwo |