Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:6 - Buku Lopatulika

6 Pamene ananena izi, analavula pansi, nakanda thope ndi malovuwo, napaka thopelo m'maso,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Pamene ananena izi, analavula pansi, nakanda thope ndi malovuwo, napaka thopelo m'maso,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Atanena zimenezi, Yesu adalavulira malovu pansi, nakanda thope ndi malovuwo. Kenaka adapaka thopelo m'maso mwa munthuyo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Atanena izi, Iye anathira malovu pansi ndi kukanda dothi, napaka matopewo mʼmaso a munthuyo.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:6
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo maso a akhungu adzatsegudwa, ndi makutu a ogontha adzatsegulidwa.


Ndipo anampatula pa khamu la anthu pa yekha, nalonga zala zake m'makutu mwake, nalavula malovu, nakhudza lilime lake:


Ndipo anamgwira dzanja munthu wakhunguyo, natulukira naye kunja kwa mudzi; ndipo atamthira malovu m'maso mwake, naika manja pa iye, anamfunsa, Uona kanthu kodi?


Iyeyu anayankha, Munthuyo wotchedwa Yesu anakanda thope, napaka m'maso mwanga, nati, kwa ine, Muka ku Siloamu kasambe; chifukwa chake ndinachoka, ndipo m'mene ndinasamba ndinapenya.


ndikulangiza ugule kwa Ine golide woyengeka m'moto, kuti ukakhale wachuma, ndi zovala zoyera, kuti ukadziveke, ndi kuti manyazi a usiwa wako asaoneke; ndi mankhwala opaka m'maso mwako, kuti ukaone.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa