Yohane 9:32 - Buku Lopatulika32 Kuyambira pachiyambi sikunamveke kuti wina anatsegulira maso munthu wosaona chibadwire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Kuyambira pachiyambi sikunamveka kuti wina anatsegulira maso munthu wosaona chibadwire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Nkale lomwe sikudamveke konse kuti wina adapenyetsa munthu wakhungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. Onani mutuwo |