Yohane 9:3 - Buku Lopatulika3 Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Yesu adati, “Sikuti iyeyu adachimwa kapena makolo ake ai. Koma adabadwa wakhungu kuti Mulungu aonetse ntchito zake mwa iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yesu anayankha kuti, “Sikuti iyeyu anachimwa kapena makolo ake, koma izi zinachitika kuti Mulungu aonetse ntchito zake mwa iyeyu. Onani mutuwo |