Yohane 9:29 - Buku Lopatulika29 Tidziwa ife kuti Mulungu analankhula ndi Mose; koma sitidziwa kumene achokera ameneyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Tidziwa ife kuti Mulungu analankhula ndi Mose; koma sitidziwa kumene achokera ameneyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Tikudziŵa kuti Mulungu adalankhula ndi Mose, koma uyu sitikudziŵa kumene wachokera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ife tikudziwa kuti Mulungu anayankhula kwa Mose, koma za munthu uyu, ife sitikudziwa ngakhale kumene akuchokera.” Onani mutuwo |