Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:27 - Buku Lopatulika

27 Iye anayankha iwo, Ndinakuuzani kale, ndipo simunamve; mufuna kumvanso bwanji? Kodi inunso mufuna kukhala ophunzira ake?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Iye anayankha iwo, Ndinakuuzani kale, ndipo simunamva; mufuna kumvanso bwanji? Kodi inunso mufuna kukhala ophunzira ake?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Iye adati, “Ndakuuzani kale, koma simumasamalako. Nanga chifukwa chiyani mukufuna kuzimvanso? Kapenatu nanunso mukufuna kukhala ophunzira ake eti?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Iye anayankha kuti, “Ine ndakuwuzani kale ndipo inu simunamvetsetse. Chifukwa chiyani mukufuna mumvenso? Mukufuna kuti inu mukhale ophunzira akenso?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:27
4 Mawu Ofanana  

nanena, Ngati uli Khristu, utiuze. Ndipo anati kwa iwo, Ndikakuuzani, simudzavomereza;


Indetu, indetu, ndinena kwa inu, kuti ikudza nthawi, ndipo ilipo tsopano, imene akufa adzamva mau a Mulungu; ndipo iwo akumva adzakhala ndi moyo.


Chifukwa chake anati kwa iye, Anakuchitira iwe chiyani? Anakutsegulira iwe maso bwanji?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa