Yohane 9:26 - Buku Lopatulika26 Chifukwa chake anati kwa iye, Anakuchitira iwe chiyani? Anakutsegulira iwe maso bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Chifukwa chake anati kwa iye, Anakuchitira iwe chiyani? Anakutsegulira iwe maso bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Iwo adamufunsa kuti, “Kodi anachita chiyani pamene anakupenyetsa?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Kenaka anamufunsa kuti, “Kodi Iye anachita chiyani kwa iwe? Iye anatsekula motani maso ako?” Onani mutuwo |