Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:23 - Buku Lopatulika

23 Chifukwa cha ichi atate wake ndi amake anati, Ali wamsinkhu; mumfunse iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Chifukwa cha ichi atate wake ndi amake anati, Ali wamsinkhu; mumfunse iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Nchifukwa chake makolo akewo adati, “Ngwamkulu, mufunseni mwiniwakeyu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Ichi ndi chifukwa chake makolo ake anati, “Mufunseni iye ndi wamkulu.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:23
2 Mawu Ofanana  

koma sitidziwa uno apenyera tsopano; kapena sitimdziwa mene anamtsegulira pamaso pake; mumfunse iye; ali wamsinkhu; adzalankhula mwini za iye yekha.


Pamenepo anamuitana kachiwiri munthuyo amene anali wosaona, nati kwa iye, Lemekeza Mulungu; tidziwa kuti munthuyo ali wochimwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa