Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo apenya bwanji tsopano? Atate wake ndi amake anayankha nati, Tidziwa kuti uyu ndi mwana wathu, ndi kuti anabadwa wosaona;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo apenya bwanji tsopano? Atate wake ndi amake anayankha nati, Tidziwa kuti uyu ndi mwana wathu, ndi kuti anabadwa wosaona;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Makolo ake adati, “Chimene tikudziŵa ife nchakuti ameneyu ndi mwana wathu, ndipo adaabadwadi wosapenya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Makolo anayankha kuti, “Ife tikudziwa kuti ndi mwana wathu, ndipo tikudziwa kuti anabadwa wosaona.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:20
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anafunsa atate wake, kuti, Chimenechi chinayamba kumgwira liti? Ndipo anati, Chidamyamba akali mwana.


nawafunsa iwo, nanena, Kodi uyu ndi mwana wanu, amene inu munena kuti anabadwa wosaona?


koma sitidziwa uno apenyera tsopano; kapena sitimdziwa mene anamtsegulira pamaso pake; mumfunse iye; ali wamsinkhu; adzalankhula mwini za iye yekha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa