Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 9:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo popita, anaona munthu ali wosaona chibadwire.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo popita, anaona munthu ali wosaona chibadwire.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Pamene Yesu ankayenda, adaona munthu wa khungu lobadwa nalo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Iye akuyendabe, anaona munthu wosaona chibadwire.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 9:1
12 Mawu Ofanana  

Pamenepo maso a akhungu adzatsegudwa, ndi makutu a ogontha adzatsegulidwa.


Ndipo onani, anthu akhungu awiri anakhala m'mphepete mwa njira; m'mene iwo anamva kuti Yesu analikupitirirapo, anafuula nati, Mutichitire ife chifundo, Inu Mwana wa Davide.


Ndipo popita Yesu kuchokera kumeneko, anamtsata Iye anthu awiri akhungu, ofuula ndi kuti, Mutichitire ife chifundo, mwana wa Davide.


Ndipo Iye anafunsa atate wake, kuti, Chimenechi chinayamba kumgwira liti? Ndipo anati, Chidamyamba akali mwana.


Ndipo mkazi, anali ndi nthenda yachidwalire zaka khumi ndi ziwiri, amene adasudzula asing'anga za moyo wake zonse, ndipo sanathe kuchiritsidwa ndi mmodzi yense,


Koma panali munthu wina apo, ali m'kudwala kwake zaka makumi atatu kudza zisanu ndi zitatu.


Pamenepo anatola miyala kuti amponye Iye; koma Yesu anabisala, natuluka mu Kachisi.


Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona?


Ndipo pa Listara panakhala munthu wina wopanda mphamvu ya m'mapazi mwake, wopunduka chibadwire, amene sanayende nthawi zonse.


Koma pamene akunjawo anaona chilombocho chili lende padzanja lake, ananena wina ndi mnzake, Zoona munthuyu ndiye wambanda. Angakhale anapulumuka m'nyanja, chilungamo sichimlola akhale ndi moyo.


Pakuti anali wa zaka zake zoposa makumi anai munthuyo, amene chizindikiro ichi chakumchiritsa chidachitidwa kwa iye.


Ndipo anapeza kumeneko munthu dzina lake Eneya, amene anagonera pamphasa zaka zisanu ndi zitatu; amene anagwidwa manjenje.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa