Yohane 9:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo popita, anaona munthu ali wosaona chibadwire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo popita, anaona munthu ali wosaona chibadwire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Yesu ankayenda, adaona munthu wa khungu lobadwa nalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Iye akuyendabe, anaona munthu wosaona chibadwire. Onani mutuwo |