Yohane 8:59 - Buku Lopatulika59 Pamenepo anatola miyala kuti amponye Iye; koma Yesu anabisala, natuluka mu Kachisi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201459 Pamenepo anatola miyala kuti amponye Iye; koma Yesu anabisala, natuluka m'Kachisi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa59 Pamenepo Ayuda aja adayamba kutola miyala kuti amlase. Koma Yesu adazemba natuluka m'Nyumba ya Mulunguyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero59 Pamenepo iwo anatola miyala kuti amugende, koma Yesu anabisala, nachoka mozemba mʼNyumba ya Mulungu. Onani mutuwo |