Yohane 8:51 - Buku Lopatulika51 Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Munthu akasunga mau anga, sadzaona imfa nthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Munthu akasunga mau anga, sadzaona imfa nthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Ndithu ndikunenetsa kuti munthu akamvera mau anga, sadzafa konse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” Onani mutuwo |