Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 8:10 - Buku Lopatulika

10 Koma Yesu pamene adaweramuka, anati kwa iye, Mkazi iwe, ali kuti ajawa? Palibe munthu anakutsutsa kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Koma Yesu pamene adaweramuka, anati kwa iye, Mkazi iwe, ali kuti ajawa? Palibe munthu anakutsutsa kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Kenaka Yesu adaŵeramuka namufunsa kuti, “Kodi mai, ali kuti anthu aja? Kodi palibe ndi mmodzi yemwe amene wakuzengani mlandu?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Yesu anaweramuka ndipo anamufunsa iye kuti, “Akuluakulu aja ali kuti? Kodi palibe amene wakutsutsa?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 8:10
3 Mawu Ofanana  

Koma pamene anakhalakhala alikumfunsabe Iye, anaweramuka, nati kwa iwo, Amene mwa inu ali wopanda tchimo, ayambe kumponya mwala.


Koma iwo, m'mene anatulukamo amodziamodzi, kuyambira akulu, kufikira otsiriza; ndipo Yesu anatsala yekha, ndi mkazi, alikuima pakati.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa