Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:2 - Buku Lopatulika

2 Koma chikondwerero cha Ayuda cha Misasa, linayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Koma chikondwerero cha Ayuda cha Misasa, linayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Nthaŵiyo nkuti chikondwerero cha Misasa chili pafupi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Koma phwando la Ayuda lamisasa litayandikira,

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:2
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu onse a Israele anasonkhana kwa mfumu Solomoni kukadyerera m'mwezi wa Etanimu, ndiwo mwezi wachisanu ndi chiwiri.


Ndipo nthawi yomweyo Solomoni anachita madyerero pamaso pa Yehova Mulungu wathu, ndi Israele yense pamodzi naye, msonkhano waukulu wakuyambira polowera ku Hamati kufikira ku nyanja ya ku Ejipito, masiku asanu ndi awiri, ndi masiku asanu ndi awiri ena, ndiwo masiku khumi mphambu anai.


Nachita chikondwerero cha Misasa monga kwalembedwa, napereka nsembe yopsereza tsiku ndi tsiku mawerengedwe ake, monga mwa lamulo lake la tsiku lake pa tsiku lake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa