Yohane 7:2 - Buku Lopatulika2 Koma chikondwerero cha Ayuda cha Misasa, linayandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma chikondwerero cha Ayuda cha Misasa, linayandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nthaŵiyo nkuti chikondwerero cha Misasa chili pafupi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma phwando la Ayuda lamisasa litayandikira, Onani mutuwo |