Yohane 6:41 - Buku Lopatulika41 Chifukwa chake Ayuda anang'ung'udza za Iye, chifukwa anati, Ine ndine mkate wotsika Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Chifukwa chake Ayuda anang'ung'udza za Iye, chifukwa anati, Ine ndine mkate wotsika Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Pamenepo Ayudawo adayamba kung'ung'udza chifukwa Yesu adaati, “Ine ndine chakudya chotsika kuchokera Kumwamba.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Pamenepo Ayuda anayamba kungʼungʼudza chifukwa anati, “Ine ndine chakudya chotsika kuchokera kumwamba.” Onani mutuwo |