Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo pamene anampeza Iye tsidya lina la nyanja, anati kwa Iye, Rabi, munadza kuno liti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo pamene anampeza Iye tsidya lina la nyanja, anati kwa Iye, Rabi, munadza kuno liti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Pamene anthu aja adampeza Yesu kutsidya kwa nyanja, adamufunsa kuti, “Aphunzitsi, mudafika liti kuno?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Atamupeza mbali ina ya nyanjayo, iwo anamufunsa Iye kuti, “Rabi, mwafika nthawi yanji kuno?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:25
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene iwo anaoloka, anafika kumtunda, ku Genesarete.


ndi kulonjeredwa m'misika, ndi kutchedwa ndi anthu, Rabi.


Koma inu musatchedwa Rabi; pakuti Mphunzitsi wanu ali mmodzi, ndipo inu nonse muli abale.


Ndipo ataoloka iwo, anafika pamtunda ku Genesarete, nakocheza padooko.


Pa mphindikati iyi ophunzira ake anampempha Iye, ndi kunena, Rabi, idyani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa