Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 6:24 - Buku Lopatulika

24 chifukwa chake pamene khamu la anthu linaona kuti palibe Yesu, ndi ophunzira ake palibe, iwo okha analowa m'ngalawazo nadza ku Kapernao, alikufuna Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 chifukwa chake pamene khamu la anthu linaona kuti palibe Yesu, ndi ophunzira ake palibe, iwo okha analowa m'ngalawazo nadza ku Kapernao, alikufuna Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Khamu lija lidaona kuti Yesu kulibe, ophunzira ake omwe kulibenso. Tsono anthu onsewo adaloŵa m'zombo zija, napita ku Kapernao kunka nafunafuna Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Nthawi yomwe gulu la anthu linaona kuti Yesu kapena ophunzira ake sanali pamenepo, ilo linalowanso mʼmabwatowo ndi kupita ku Kaperenawo kukamufunafuna Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:24
11 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene iwo anaoloka, anafika kumtunda, ku Genesarete.


nampeza, nanena naye, Akufunani Inu anthu onse.


Ndipo ataoloka iwo, anafika pamtunda ku Genesarete, nakocheza padooko.


Ndipo pakubwera Yesu, khamu la anthu linamlandira Iye; pakuti onse analikumlindira Iye.


Yesu ananena naye, Mkazi, uliranji? Ufuna yani? Iyeyu poyesa kuti ndiye wakumunda, ananena ndi Iye, Mbuye ngati mwamnyamula Iye, ndiuzeni kumene mwamuika Iye, ndipo ndidzamchotsa.


ndipo pamene adalowa m'ngalawa, analikuoloka nyanja kunka ku Kapernao. Ndipo kutada pamenepo, koma Yesu asanadze kwa iwo.


koma zinachokera ngalawa zina ku Tiberiasi, pafupi pamalo pomwe adadyapo mkate m'mene Ambuye Yesu adayamika;


Yesu anayankha iwo nati, Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Mundifuna Ine, si chifukwa munaona zizindikiro, koma chifukwa munadya mkate, nimunakhuta.


Izi ananena m'sunagoge, pakuphunzitsa mu Kapernao.


Pomwepo Ayuda analikumfuna Iye pachikondwerero, nanena, Ali kuti uja?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa